Return to BahaiPrayers.net
Facebook
O Mulungu! Phunzitsani ana awa. Ana awa ali zomera za m’munda Wanu wazipatso, maluwa a M’dimba Lanu, Lozesi wa m’munda Wanu. Lolani kuti mvula Yanu iwagwere; lolani kuti dzuwa la choonadi liwalire pa iwo ndi chikondi Chanu. Lolani kuti mweya Wanu uwatsitsimutse mwakuti iwo aphunzitsidwe, akule ndipo adzadziwe, ndi kuoneka okongola kweni-kweni. Inu Ndinu Wopatsa. Inu Ndinu Wachisoni.
- `Abdu'l-Bahá