Return to BahaiPrayers.net
Facebook
O Ambuye wanga! Pangani kukongola Kwanu kukhale chakudya changa, ndikupezeka Kwanu ndi chakumwa changa ndipo chitamando Chanu ndiye kuchita kwanga ndipo kukumbukira Inu ndiye mzanga, ndipo mphamvu ya Ulumuliro Wanu ndi chithandizo changa, malo Amene Mukhala ndi ku khomo kwanga, ndipo malo anga omwe ndikhala ndi malo omwe inu mwawadalitsa kuchokera ku muyeso umene mwaupereka kwa iwo amene azitsekera poziphimba kwa inu. Inu ndinu, ndithudi, wamkulu, wa ulemelero onse, wamphamvu zonse.”
- Bahá'u'lláh